The Very Best - Nsokoto paroles de chanson

paroles de chanson Nsokoto - The Very Best



Kumsokoto kuli mfiti imodzi inkalodza ana osalakwa
Kupata kwa ana iyo sinkasangalatsidwa nako
Mwana apate eti tiona ngati agone
Chaka chino chokha iye akagonera kumanda
M'mati n'kwere ndakwera panyumba yanthakati
Wakoma bana pawaka
Wamara bana nsokoto
Mwana akangoti agone
Kum'bwerera usiku
Thupi lonse lamangika
Kulephera kufuula
Poti adsuke mam'mawa
Thupi kunjenjemera
Mutu wanga, malungo, matenda aja akula
Wakoma bana
Wati kitasha
Wamara bana
Ichi n'chasoni
Nsokoto nsokoto
Nsokoto nsokoto
Muuze nthakatiyo namulondola ife takana
Bana bakunsokoto ise
Bana bakumulowe ise
Bana bamwakisulu ise
Bana bakaronga ise
Bana bakurumphi ise
Bana bakuchitipa ise



Writer(s): Esau Mwamwaya, Johan Karlberg, Etienne Tron De Bouchony De Berard De


The Very Best - Warm Heart of Africa
Album Warm Heart of Africa
date de sortie
14-09-2009




Attention! N'hésitez pas à laisser des commentaires.