Текст песни




Osanisiya iwe eeh
Kulibe malu iwe
Kwina ningapeze
Oh nikonda, no
Osanisiya iwe eeh
Kulibe malu iwe
Kwina ningapeze
Oh nikonda, no
Tekanya iwe, bika m'tima pansi
After nakamba ve niza kamba
Ungachite ve ufuna
Siubiza ati masiku yano bantu bataamba
Vonse tima chita iwe
Nakonse tima eenda
Ninga kambe namukhazi uli onse koma
Story unzamvela izapindamuka mukamwaya muntu
Osanisiya iwe eeh
Kulibe malu iwe
Kwina ningapeze
Oh nikonda, no
Osanisiya iwe eeh
Kulibe malu iwe
Kwina ningapeze
Oh nikonda, no
Kambili ine nimamvela pili ipita mu chalo
Ungankale nawapambali iwe, maninga kunyumba usova
So lelo nifuna ati uni onesese iwe
Kuti ine umoyo wanga na mukati monse
Unatenga elo iwe siningakusiye
Olo chivute bwanji
Ndiwe chabe weka
Osanisiya iwe eeh
Kulibe malu iwe
Kwina ningapeze
Oh nikonda, no
Osanisiya iwe eeh
Kulibe malu iwe
Kwina ningapeze
Oh nikonda, no
Nifuna niku mvesese pasiku ya lelo, iwe
Usawale awe, siningakusiye, iwe
Nifuna niku mvesese pasiku ya lelo, iwe
Usawale awe, siningakusiye, iwe
Olo chivute bwanji, iwe
Siningakusiye awe, ine
Olo chivute bwanji, iwe
Siningakusiye awe, ine
Osanisiya iwe eeh
Kulibe malu iwe
Kwina ningapeze
Oh nikonda, no
Osanisiya iwe eeh
Kulibe malu iwe
Kwina ningapeze
Oh nikonda, no
Osanisiya iwe eeh
Kulibe malu iwe
Kwina ningapeze
Oh nikonda, no
Osanisiya iwe eeh
Kulibe malu iwe
Kwina ningapeze
Oh nikonda, no
Osanisiya iwe eeh
Kulibe malu iwe
Kwina ningapeze
Oh nikonda, no
Osanisiya iwe eeh
Kulibe malu iwe
Kwina ningapeze
Oh nikonda, no





Внимание! Не стесняйтесь оставлять отзывы.
Загрузка
Загрузка