Gwamba - Mtima Pansi (feat. Onesimus) текст песни

Текст песни Mtima Pansi (feat. Onesimus) - Gwamba



Uyike ntima pansi
Usadandaule khala pansi
Zonse ndi nthawi basi
Usamasweke ntima n'zinthu zazing'ono
Gwada Yehova akugwile nkono
Tadekha Tadekha
Yeeeeiiieeeeh
Aaaa aaaa aaaa aaaaah
Oooo oooo ooooh ooh oh
Uh!!
Gwada kwa Ambuye ndi mavuto ako
Akafuna kuyankha samafunsa nzako
Muuze zonse zokhumba za ntima wako
Ndi wamkulu heavy kuposa vuto lako
Eish!
Ndiyekhayo yemwe angakukonze
Anawolotsa nyanja achina Mose
Akhale patsogolo zinthu zonse
Olo utachimwa buanj akudzodze
Osadanda mphanga izi nzazing'ono
Yehova wakumwamba ali ndi chisomo
Ika manja m'mwamba akugwile nkono
Uyike ntima pansi
Usadandaule khala pansi
Zonse ndi nthawi basi
Usamasweke ntima n'zinthu zazing'ono
Gwada Yehova akugwile nkono
Tadekha Tadekha
Aaaahh aaaah aaah aaahh
Oooo ooooh ooooh oooh
Uh! mwetulira mphwanga usanyasitse nkhope
Akachedwa kuyankha usatope
Umawelenga Bible?
Ana a Mulungu anayenda pansi
Kwa zaka 40
Mlaliki paguwa kulalikira agonthi
Maso patsogolo iwe si Mkazi wa Loti
Panyanja yamachimo pati floater
Ngati boat
Machimo mu ntima mwako kupanga deport
Eish! Mphepo yaukali
Yahwe akugwila nkono ufika kutali
Ndati, mphepo yaukali
Akayendetsa Yahwe moyo wako
N'wawutali
Uyike ntima pansi
Usadandaule khala pansi
Zonse ndi nthawi basi
Usamasweke ntima n'zinthu zazing'ono
Gwada Yehova akugwile nkono
Tadekha Tadekha
Yeeeiiiyeeee
Aaaah aaah aaaah aaaaaaah
Ooooh oooh ohhhhh!




Gwamba - Mama Said God First
Альбом Mama Said God First
дата релиза
29-09-2019




Внимание! Не стесняйтесь оставлять отзывы.